LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 October tsa. 6
  • ‘Muzikumbukila Nthawi Zonse Kubwela Kwa Tsiku la Yehova’

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • ‘Muzikumbukila Nthawi Zonse Kubwela Kwa Tsiku la Yehova’
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • “Mukhale Oyela”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Yehova Analenga Zamoyo pa Dziko Lapansi
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Ambili Adzapulumuka—Nanga Bwanji Inuyo?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Kudzipeleka kwa Mulungu Kapena ku Cuma
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 October tsa. 6

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 2 PETULO 1-3

‘Muzikumbukila Nthawi Zonse Kubwela Kwa Tsiku la Yehova’

3:11, 12

Yehova sadzazengeleza kuweluza anthu mwacilungamo pa nthawi yake. Kodi zocita zathu zimaonetsa kuti talikonzekela tsiku la Yehova?

Kodi kukhala na ‘khalidwe loyela ndiponso kucita nchito zosonyeza kuti ndinu odzipeleka kwa Mulungu’ kutanthauza ciani?

  • Tifunika kukhala oyela m’makhalidwe athu ndiponso kuteteza cikhulupililo cathu

  • Nthawi zonse tiyenela kucita zinthu mogwilizana na kulambila kwathu, kaya pagulu kapena kwatokha

Mwamuna na mkazi wake akuganizila mmene umoyo wawo unalili pamene anali kuthela nthawi yoculuka pa kutamba TV na kugula zinthu, ndipo akuuyelekezela na mmene ulili tsopano cifukwa cotengako mbali pocita ulaliki wapoyela na kulambila kwa pabanja

Ningaonetse bwanji kuti nimakumbukila tsiku la Yehova nthawi zonse?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani