LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 April tsa. 5
  • Kodi Mukulimbikila kuti Mupeze Madalitso?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Mukulimbikila kuti Mupeze Madalitso?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Cilimikani pa Kulimbana Kuti Mupeze Madalitso a Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
  • Kodi Cofunika Koposa kwa Ine N’ciani?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • “Musamade Nkhawa ndi Kanthu Kalikonse”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Yakobo Analandila Madalitso Omuyenelela
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 April tsa. 5

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 32-33

Kodi Mukulimbikila kuti Mupeze Madalitso?

32:24-28

Kuti tilandile dalitso la Yehova, tifunika kulimbikila kuika zinthu za Ufumu patsogolo mu umoyo wathu. (1 Akor. 9:26, 27) Pamene titumikila Yehova, tiyenela kukhala na mzimu umene Yakobo anaonetsa polimbana na mngelo. Tingaonetse kuti tifuna dalitso la Yehova mwa . . .

  • Kukonzekela bwino misonkhano ya mpingo

  • Kutengako mbali nthawi zonse mu ulaliki

  • Kuyesetsa kuthandiza ena mumpingo

Zithunzi: Mayi amene amakhala na zocita zambili. 1. Akupemphela m’mawa asanayambe kucita ciliconse. 2. Akudyetsa mwana wake asanapite mu ulaliki. 3. Akugwila nchito yolalikila mosangalala pamodzi na ana ake aŵili komanso alongo ena a mumpingo wake.

Olo kuti zinthu n’zovuta mu umoyo wanu, osaleka kupemphela kwa Yehova kuti akuthandizeni. Komanso, limbikilani pom’tumikila ndipo adzakudalitsani.

Dzifunseni kuti: ‘Mu umoyo wanga, ni mbali ziti zimene nifunika kulimbikilapo kuti nilandile dalitso la Yehova?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani