LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 148
  • Yehova Amapulumutsa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova Amapulumutsa
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Amapereka Chipulumutso
    Imbirani Yehova
  • Nilimbitseni Mtima
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Cuma Capadela
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Cuma Capadela
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 148

NYIMBO 148

Yehova Amapulumutsa

Yopulinta

(2 Samueli 22:1-8)

  1. 1. Yehova, ndimwedi Mulungu wamoyo;

    Ndimwe munalenga

    kumwamba na dziko.

    Ndani angalimbane namwe M’lungu?

    Kulibe.

    Adani adziŵe.

    (KOLASI)

    Yehova M’lungu wathu m’pothaŵila.

    Iye ni Thanthwe kwa atumiki ake.

    Tisayope, tilimbe mtima.

    Dzina lake tilengeze pa dziko lonse,

    tim’tamande.

  2. 2. Ngakhale kuti nizingidwe na imfa,

    Atate Yehova,

    nipatseni mphamvu.

    Nilimbitseni mtima,

    n’tetezeni,

    Nipempha, conde M’lungu wanga.

    (KOLASI)

    Yehova M’lungu wathu m’pothaŵila.

    Iye ni Thanthwe kwa atumiki ake.

    Tisayope, tilimbe mtima.

    Dzina lake tilengeze pa dziko lonse,

    tim’tamande.

  3. 3. Kucokela kumwamba mudzabangula.

    Olimbana namwe

    adzati nje nje nje.

    Koma okukondani

    adzakondwa

    Cifukwa adzapulumuka.

    (KOLASI)

    Yehova M’lungu wathu m’pothaŵila.

    Iye ni Thanthwe kwa atumiki ake.

    Tisayope, tilimbe mtima.

    Dzina lake tilengeze pa dziko lonse,

    tim’tamande.

(Onaninso Sal. 18:1, 2; 144:1, 2.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani