LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 13
  • Khristu ni Citsanzo Cathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khristu ni Citsanzo Cathu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Muzicita Zinthu Mogwilizana ndi Pemphelo Lacitsanzo—Mbali 1
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • ‘Tsatilani Mapazi Ake Mosamala Kwambili’
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Khristu Ndi Chitsanzo Chathu
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 13

NYIMBO 13

Khristu ni Citsanzo Cathu

Yopulinta

(1 Petulo 2:21)

  1. 1. Timayamikila,

    Cikondi ca M’lungu—

    Anapeleka Yesu Mwana wake.

    Khristu’a naonetsa,

    Citsanzo cabwino—

    Anayeletsa dzina Ia M’lungu.

  2. 2. Mau a Yehova,

    Anamuthandiza,

    Kuti akhale wokhulupilika.

    Anatumikila

    M’lungu mokondwela,

    Tidzatengela citsanzo cake.

  3. 3. Khristu’a natipatsa

    Citsanzo cabwino—

    Anatamanda Yehova Atate.

    Ise tilengeze

    Ufumu wa M’lungu.

    Tidzalandila moyo wosatha.

(Onaninso Yoh. 8:29; Aef. 5:2; Afil. 2:5-7)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani