LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 7
  • Yehova Ndiye Mphamvu Zathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova Ndiye Mphamvu Zathu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Ndiye Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova
  • Mvelani Pemphelo Langa Conde
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mulungu Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova
  • Funani Cipulumutso ca Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 7

NYIMBO 7

Yehova Ndiye Mphamvu Zathu

Yopulinta

(Yesaya 12:2)

  1. 1. M’lungu wathu ndimwe mphamvu zathu.

    Imwe ndimwe mpulumutsi wathu.

    Timalengeza uthenga wanu,

    Ngakhale kuti ena samvela.

    (KOLASI)

    Yehova ndimwe wamphamvuzonse.

    Timadziŵitsa dzina lanu.

    Yehova timakudalilani.

    Ndimwe mphamvu zathu—nsanja yathu.

  2. 2. Mwationetsa kuwala kwanu.

    M’lungu mwatiphunzitsa co’nadi.

    Mu Mau anu tipeza nzelu;

    Ise tasankha Ufumu wanu.

    (KOLASI)

    Yehova ndimwe wamphamvuzonse.

    Timadziŵitsa dzina lanu.

    Yehova timakudalilani.

    Ndimwe mphamvu zathu—nsanja yathu.

  3. 3. Timatumikila mokondwela,

    Ngakhale Satana ‘tivutitse.

    Ngakhale tikumane na imfa

    Ise tidzamvela imwe cabe.

    (KOLASI)

    Yehova ndimwe wamphamvuzonse.

    Timadziŵitsa dzina lanu.

    Yehova timakudalilani.

    Ndimwe mphamvu zathu—nsanja yathu.

(Onaninso 2 Sam. 22:3; Sal. 18:2; Yes. 43:12.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani