LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 66
  • Lengezani Uthenga Wabwino

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Lengezani Uthenga Wabwino
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Lalikirani Uthenga Wabwino
    Imbirani Yehova
  • Cuma Capadela
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Cuma Capadela
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • “Uthenga Wabwino”!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 66

NYIMBO 66

Lengezani Uthenga Wabwino

Yopulinta

(Chivumbulutso 14:6, 7)

  1. 1. Kale anthu sanadziŵe za Ufumu.

    Koma lomba na Mfumu yake tidziŵa.

    Mwa cifundo cake Atate Yehova,

    Anaganizila anthu ocimwafe.

    Anafuna Khristu adzalamulile;

    Panthawi yake,

    Ufumuwo unabadwa.

    Anasankha ena kudzalamulila

    Pamodzi na mwana wake Khristu Mfumu.

  2. 2. Cinali cifuno ca Yehova M’lungu.

    Kuti uthengawu ukalalikidwe.

    Angelo akondwa kutsagana nafe,

    Kutithandiza kulengeza Ufumu.

    Ni mwayi kukhala Mboni za Yehova.

    Kuyeletsa dzina lake

    na kum’tamanda.

    Timalemekeza nchito yathu iyi

    Yolengeza uthenga kwa anthu onse.

(Onaninso Maliko 4:11; Mac. 5:31; 1 Akor. 2:1, 7.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani