LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 28
  • Kukhala Bwenzi la Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kukhala Bwenzi la Yehova
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tikhale pa Ubwenzi ndi Yehova
    Imbirani Yehova
  • Mulungu Akupemphani Kuti Mukhale Mnzake
    Na Imwe Mungakhale Mnzake wa Mulungu!
  • Mukhoza Kukhala Bwenzi la Yehova
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
  • Yehova Ndi Bwenzi Lathu Lapamtima
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 28

NYIMBO 28

Kukhala Bwenzi la Yehova

Yopulinta

(Salimo 15)

  1. 1. Ndani angakhale

    Bwenzi lanu M’lungu?

    Ndani mungakhulupilile?

    Angakudziŵeni?

    Ni uja amene

    Amakumvelani.

    Komanso wokhulupilika,

    Wokonda co’nadi.

  2. 2. Ndani angakhale

    Bwenzi lanu M’lungu?

    Ndani amene mungakonde

    Nakumudalitsa?

    Ni uja amene

    Amakukwezani.

    Iye amanena zoona,

    Ni woona mtima.

  3. 3. Nkhawa zathu zonse

    Timakuuzani.

    Ndipo mumatisamalila,

    Tsiku lililonse.

    Tifuna kukhala

    Bwenzi lanu M’lungu.

    Palibe bwenzi tingapeze

    Monga inu M’lungu.

(Onaninso Sal. 139:1; 1 Pet. 5:6, 7.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani