LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 45
  • Kusinkha-sinkha kwa Mtima Wanga

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kusinkha-sinkha kwa Mtima Wanga
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Kusinkhasinkha kwa Mtima Wanga
    Imbirani Yehova
  • “Pitilizani Kuganizila Zimenezi”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 45

NYIMBO 45

Kusinkha-sinkha kwa Mtima Wanga

Yopulinta

(Salimo 19:14)

  1. 1. Zonse za mu mtima wanga,

    Zimene nimaganiza—

    Zikhale zokondweletsa

    Imwe Ambuye Yehova.

    Pamene nili na nkhawa,

    Na tulo osatuona,

    Nisinkhe-sinkhe za imwe

    Na pa zinthu zolungama.

  2. 2. Pa zilizonse zoyela,

    Na zilizonse zoona,

    Pa zonse zotamandika—

    Ine nidzaganizila.

    Maganizo anu M’lungu

    Amanipatsa mtendele.

    Ine niwasinkhe-sinkhe,

    Pa iwo niganizile.

(Onaninso Sal. 49:3; 63:6; 139:17, 23; Afil. 4:7, 8; 1 Tim. 4:15)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani