LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 98
  • Malemba ni Ouzilidwa na Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Malemba ni Ouzilidwa na Mulungu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Malemba Anauziridwa ndi Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo ni Cozizwitsa
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 98

NYIMBO 98

Malemba ni Ouzilidwa na Mulungu

Yopulinta

(2 Timoteyo 3:16, 17)

  1. 1. Mu dziko ili la mdima,

    Timaona kuwala,

    Kwa Mau a M’lungu wathu,

    Opezeka mu Baibo.

  2. 2. Yehova anatipatsa

    Mau ouzilidwa.

    Kuti atitsogolele

    Mu njila ya cilungamo.

  3. 3. Mau a Yehova M’lungu

    Amatilimbikitsa.

    Iye ni Atate wathu,

    Tidziŵa amatikonda.

(Onaninso Sal. 119:105; Miy. 4:13.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani