LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 6
  • Zakumwamba Zilengeza Ulemelelo wa Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zakumwamba Zilengeza Ulemelelo wa Mulungu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Zakumwamba Zimalengeza Ulemerero wa Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Zolengedwa Zimasonyeza Ulemerero wa Yehova
    Imbirani Yehova
  • Cilengedwe Citamanda Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • M’patseni Ulemelelo Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 6

NYIMBO 6

Zakumwamba Zilengeza Ulemelelo wa Mulungu

Yopulinta

(Salimo 19)

  1. 1. Zakumwamba zitamanda Yehova.

    Zilengeza mphamvu

    zake zodabwitsa.

    Dzuŵa, mwezi na nyenyezi zonse

    Zimationetsa nzelu

    Na cikondi cake.

  2. 2. Malamulo a M’lungu ni angwilo,

    Amapatsa moyo

    kwa oŵatsatila.

    Ziweluzo zake n’zolungama.

    Mau ake ni oyela,

    Amatsitsimula.

  3. 3. Tingakhale na moyo wamuyaya,

    Ngati ’se tiopa

    Atate Yehova.

    Kumumvela kumatiteteza.

    Tiyeni tizilengeza.

    Ucifumu wake.

(Onaninso Sal. 111:9; 145: 5; Chiv. 4:11.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani