LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 46
  • Tikuyamikani Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tikuyamikani Yehova
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tikuyamikani Yehova
    Imbirani Yehova
  • Pemphelo la Mtumiki wa Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tiziyamikila Mwayi Wathu wa Pemphelo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Umoyo wa Mpainiya
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 46

NYIMBO 46

Tikuyamikani Yehova

Yopulinta

(1 Atesalonika 5:18)

  1. 1. Tiyamikila Yehova Mulungu,

    Munatipatsa kuwala kwanu.

    Tiyamikila mwayi wa pemphelo,

    Wokuuzani mavuto athu.

  2. 2. Tiyamikila munatuma Yesu,

    Anapilila mpaka mapeto.

    Tiyamikila mumatithandiza,

    Kucita zimene mumafuna.

  3. 3. Tiyamikila potipatsa mwayi,

    Wouza anthu za dzina lanu.

    Tiyamikila za Ufumu wanu,

    Kuti udzaleta madalitso.

(Onaninso Sal. 50:14; 95:2; 147:7; Akol. 3:15.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani