LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 133
  • Lambila Yehova Ukali Wacicepele

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Lambila Yehova Ukali Wacicepele
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Lambirani Yehova Muli Achinyamata
    Imbirani Yehova
  • Timam’konda Kwambili Atate Wathu Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 133

NYIMBO 133

Lambila Yehova Ukali Wacicepele

Yopulinta

(Mlaliki 12:1)

  1. 1. Ise anyamata na ‘tsikana,

    Yehova atikonda kwambili.

    Atisamalila mwacikondi;

    Adzadalitsa masiku athu.

  2. 2. Polemekeza makolo athu,

    Tionetsa kuti tiŵakonda.

    Ndipo Yehova adzatiyanja.

    Iye adzakhala bwenzi lathu.

  3. 3. Tikumbukile Yehova M’lungu,

    M’nthawi ya ucicepele wathu.

    Tim’tumikile na moyo wonse,

    Tidzakondweletsa mtima wake.

(Onaninso Sal. 71:17; Malilo 3:27; Aef. 6:1-3.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani