LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 65
  • Pita Patsogolo!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pita Patsogolo!
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Pitani Patsogolo
    Imbirani Yehova
  • “Onetsani Kuwala Kwanu”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • “Onetsani Kuwala Kwanu” Kuti Yehova Alemekezeke
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • “Lalikila Mau”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 65

NYIMBO 65

Pita Patsogolo!

Yopulinta

(Aheberi 6:1)

  1. 1. Pita patsogolo mu ulaliki!

    Walitsa co’nadi kuti onse aone.

    Ukhale na luso polalikila;

    Udalile Yehova.

    Nchito iyi ni yathu tonse;

    Na Yesu analalikila.

    Ukadalila Mulungu, sudzagwa.

    Udzakhala wolimba.

  2. 2. Pita patsogolo, ucilimike!

    Ulalikile uthenga kwa anthu onse.

    Polalikilabe khomo ndi khomo,

    Utamande Yehova.

    Olo adani akuyofye,

    Usayope lalikilabe.

    Lengeza za Ufumu wa Yehova;

    Phunzitsa coonadi.

  3. 3. Pita patsogolo, ucite cangu.

    Nola luso lako, ndipo udzapambana.

    Mzimu wa Mulungu ukuthandize.

    Udzapeza cimwemwe.

    Konda anthu omwe upeza,

    Kuti uwafike pamtima.

    Iwo akakula mwakuuzimu,

    Co’nadi cidzawala.

(Onaninso Afil. 1:27; 3:16; Aheb. 10:39.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani