LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 48
  • Kuyenda ndi Yehova Tsiku na Tsiku

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kuyenda ndi Yehova Tsiku na Tsiku
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Timayenda ndi Yehova Tsiku Lililonse!
    Imbirani Yehova
  • Uziyenda na Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Yendani ndi Mulungu!
    Imbirani Yehova
  • Tikhale Okhulupilika Nthawi Zonse
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 48

NYIMBO 48

Kuyenda ndi Yehova Tsiku na Tsiku

Yopulinta

(Mika 6:8)

  1. 1. Tiziyenda na Yehova,

    Nthawi zonse modzicepetsa.

    Apatsa cisomo cake,

    Kwa osakila njila zake.

    Iye mwa cikondi cake,

    Adzatitsogolela.

    Tidzipeleke kwa iye

    Kuti timutumikile.

  2. 2. Mapeto ayandikila,

    Ndipo Satana ni wokwiya.

    Adani amatiyofya

    Kuti tisayende na M’lungu.

    M’lungu adzatithandiza

    Kuti tiyende naye.

    Titumikile Yehova

    Mpaka umuyaya wonse.

  3. 3. Mwa Mau na mzimu wake,

    Yehova amatithandiza.

    Watipatsa mpingo wake;

    Amamvela tikapemphela.

    Yehova atithandiza

    Kucita zoyenela.

    Afuna poyenda naye

    Tikhale odzicepetsa.

(Onaninso Gen. 5:24; 6:9; 1 Maf. 2:3, 4.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani