LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 49
  • Tikondweletse Mtima wa Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tikondweletse Mtima wa Yehova
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tikondweretse Mtima wa Yehova
    Imbirani Yehova
  • Kodi Mumamvela Bwanji?
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kodi Mumamvela Bwanji?
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • “Muzitsimikizira Kuti Zinthu Zofunika Kwambiri Ndi Ziti”
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 49

NYIMBO 49

Tikondweletse Mtima wa Yehova

Yopulinta

(Miyambo 27:11)

  1. 1. Tikulonjezani M’lungu,

    Tidzakutumikilani,

    Ise timakukondani.

    Tidzakukondweletsani.

  2. 2. Atate munatipatsa

    Kapolo wanu wanzelu,

    Kuti atisamalile,

    Atiphunzitse za imwe.

  3. 3. Tipatseni mzimu wanu,

    Kuti ‘se utithandize

    Kulengeza dzina lanu,

    Kucita zofuna zanu.

(Onaninso Mat. 24:45-47; Luka 11:13; 22:42.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani