LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 122
  • Cilimikani, Musasunthike!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Cilimikani, Musasunthike!
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Khalani Olimba, Osasunthika
    Imbirani Yehova
  • “Khalani Olimba, Osasunthika”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Adzakulimbitsa
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mulungu Adzakupatsani Mphamvu
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 122

NYIMBO 122

Cilimikani, Musasunthike!

Yopulinta

(1 Akorinto 15:58)

  1. 1. Anthu avutika maganizo.

    Aopa zinthu zakutsogolo.

    Ise tisaleke, tisafo’ke,

    Titumikile M’lungu.

    (KOLASI)

    Ticilimike tonse;

    Tisakonde za m’dziko.

    Tikacilimika,

    Tidzapeza moyo.

  2. 2. Tikakumana na mayeselo,

    Tidziŵa kuti tidzapambana.

    Ngati tikonda zinthu zabwino,

    Tidzakhala olimba.

    (KOLASI)

    Ticilimike tonse;

    Tisakonde za m’dziko.

    Tikacilimika,

    Tidzapeza moyo.

  3. 3. Tilambile Yehova Mulungu.

    Tim’tumikile modzipeleka.

    Tilalikile onse mwakhama.

    Mapeto adzafika.

    (KOLASI)

    Ticilimike tonse;

    Tisakonde za m’dziko.

    Tikacilimika,

    Tidzapeza moyo.

(Onaninso Luka 21:9; 1 Pet. 4:7.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani