LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 60
  • Mulungu Adzakupatsani Mphamvu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mulungu Adzakupatsani Mphamvu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Adzakulimbitsa
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tikhale na Cikhulupililo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 60

Nyimbo 60

Mulungu Adzakupatsani Mphamvu

(1 Petulo 5:10)

1. Panali chifukwa chimene Mulungu

Anakupatsira choonadi

Anaona mtima wofuna kuchita

Zabwino zomukondweretsadi.

Unalonjeza kum’tumikira

Ndipo Iye anakuthandiza

(KOLASI)

Ndi magazi a Yesu Anakuwombola

Adzakulimbitsa adzakuteteza.

Adzakutsogolera ndi mzimu woyera

Adzakulimbitsa adzakuteteza.

2. Mulungu anapereka mwana wake

Amafunadi zikuyendere.

Ngati mwana wakeyo sanatimane

Kukulimbitsa sangalephere.

Chikondi chako sangaiwale

Sangasiye konse anthu ake.

(KOLASI)

Ndi magazi a Yesu Anakuwombola

Adzakulimbitsa adzakuteteza.

Adzakutsogolera ndi mzimu woyera

Adzakulimbitsa adzakuteteza.

(Onaninso Aroma 8:32; 14:8, 9; Aheb. 6:10; 1 Pet. 2:9.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani