LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 131
  • “Cimene Mulungu Wacimanga Pamodzi”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Cimene Mulungu Wacimanga Pamodzi”
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi”
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wosatha Watheka!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mulungu Watilonjeza Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova
  • Tidzapeza Moyo Wosatha!
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 131

NYIMBO 131

“Cimene Mulungu Wacimanga Pamodzi”

Yopulinta

(Mateyu 19:5, 6)

  1. 1. Anthu na Mulungu,

    Acita umboni,

    Za cikwati ca lelo,

    Comangidwa bwino.

    (KOLASI 1)

    Mwamuna walonjeza

    Kukonda mkaziyu.

    “Ngati M’lungu wamanga,

    Musalekanitse.”

  2. 2. Onse aphunzila,

    Mau a Yehova.

    Lomba ayembekeza,

    Dalitso la M’lungu.

    (KOLASI 2)

    Mkazinso walonjeza

    Kukonda mwamuna.

    “Ngati M’lungu wamanga,

    Musalekanitse.”

(Onaninso Gen. 2:24; Mlal. 4:12; Aef. 5:22-33.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani