Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Numeri 1:47
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Koma Alevi,+ mogwirizana ndi fuko la makolo awo, sanawawerenge pamodzi ndi anthu enawo.+

  • Numeri 26:62, 63
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 62 Onse amene anawerengedwa pakati pa Alevi analipo 23,000. Amenewa anali amuna onse kuyambira amwezi umodzi kupita mʼtsogolo.+ Iwo sanawerengedwe limodzi ndi Aisiraeli,+ chifukwa sanafunikire kulandira cholowa pakati pa Aisiraeli.+

      63 Awa ndi anthu amene Mose ndi wansembe Eleazara anawawerenga pakati pa Aisiraeli. Anawawerengera mʼchipululu cha Mowabu, pafupi ndi mtsinje wa Yorodano, kufupi ndi Yeriko.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani