Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Samueli 21:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 2 Samueli 21:20-22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kenako panayambikanso nkhondo ina ku Gati ndipo kunali munthu wamkulu modabwitsa. Iye anali ndi zala 6 kudzanja lililonse ndiponso zala 6 kuphazi lililonse, moti anali ndi zala 24. Nayenso anali mbadwa ya Arefai.+ 21 Iye ankanyoza kwambiri Aisiraeli.+ Choncho Yonatani mwana wa Simeyi,+ mchimwene wake wa Davide, anamupha.

      22 Anthu 4 amenewa anali mbadwa za Arefai ku Gati ndipo anaphedwa ndi Davide ndi atumiki ake.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani