Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Ekisodo 6:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Salimo 68:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Imbirani Mulungu, muimbireni nyimbo zotamanda dzina lake.+

      Imbirani Iye amene akudutsa mʼchipululu.*

      Dzina lake ndi Ya.*+ Sangalalani pamaso pake.

  • Yesaya 42:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 54:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Chifukwa Wokupanga Wamkulu+ ali ngati mwamuna* wako,+

      Dzina lake ndi Yehova wa magulu ankhondo akumwamba,

      Ndipo Woyera wa Isiraeli ndiye Wokuwombola.+

      Iye adzatchedwa Mulungu wa dziko lonse lapansi.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani