-
Nehemiya 2:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Kenako ndinayankha mfumuyo kuti: “Mfumu mukhale ndi moyo wautali! Ndilekerenji kuoneka wachisoni pamene mzinda umene makolo anga anaikidwako uli bwinja ndipo mageti ake anatenthedwa ndi moto?”+
-