-
Maliro 4:9Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
9 Amene anaphedwa ndi lupanga aliko bwino kusiyana ndi amene anafa ndi njala.+
Amenewa anafooka nʼkufa chifukwa chosowa chakudya ndipo anafa ngati abayidwa ndi lupanga.
-