Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 5:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pa zikondwerero zawo amaimbapo azeze, zoimbira za zingwe,

      Maseche ndi zitoliro ndipo amamwapo vinyo.

      Koma saganizira zochita za Yehova,

      Ndipo saona ntchito ya manja ake.

  • Yesaya 56:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “Tabwerani! Dikirani ndikatenge vinyo

      Ndipo timwe mpaka kuledzera.+

      Mawa lidzakhalanso ngati lero, mwinanso kuposa pamenepa.”

  • Amosi 6:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Tsoka kwa anthu amene akukhala mosatekeseka ku Ziyoni,

      Ndiponso anthu amene akuona kuti ndi otetezeka mʼphiri la Samariya.+

      Anthu olemekezeka a mtundu wotchuka kuposa mitundu ina,

      Amene nyumba yonse ya Isiraeli imapita kwa iwowo.

  • Amosi 6:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Mumagona pamabedi aminyanga ya njovu+ ndi kudziwongola pamipando yokhala ngati bedi,+

      Ndiponso mukudya nkhosa zamphongo komanso ana a ngʼombe* onenepa.+

  • Luka 17:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yakobo 5:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani