-
Deuteronomo 28:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Koma mukapanda kumvera mawu a Yehova Mulungu wanu poonetsetsa kuti mukutsatira malamulo ake onse ndi malangizo ake amene ndikukupatsani lero, mudzatembereredwa ndipo zinthu zoipa zotsatirazi zidzakuchitikirani:+
-
-
Yeremiya 9:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
21 Chifukwa imfa yatilowera mʼnyumba kudzera mʼmawindo.
Yalowa munsanja zathu zokhala ndi makoma olimba
Kuti mumsewu musapezeke mwana aliyense
Ndiponso kuti anyamata asapezeke mʼmabwalo a mzinda.’+
-
-
Ezekieli 24:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
21 ‘Uza nyumba ya Isiraeli kuti: “Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Ndatsala pangʼono kudetsa malo anga opatulika,+ chinthu chimene mumachinyadira kwambiri, chinthu chimene mumachikonda komanso chapamtima panu. Ana anu aamuna ndi aakazi amene munawasiya mumzindawo adzaphedwa ndi lupanga.+
-