Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Hoseya 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndidzawononga mitengo yake ya mpesa ndi ya mkuyu imene iye wanena kuti:

      “Amenewa ndi malipiro amene amuna ondikonda kwambiri anandipatsa.”

      Koma ine mitengoyo ndidzaisandutsa kukhala nkhalango,

      Ndipo zilombo zakutchire zidzaidya.

  • Mika 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Zifaniziro zake zonse zogoba zidzaphwanyidwa nʼkukhala zidutswazidutswa.+

      Ndipo mphatso zonse zimene ankalandira ngati malipiro zidzatenthedwa pamoto.+

      Mafano ake onse ndidzawawononga.

      Chifukwa anawapeza kuchokera ku ndalama zimene ankalandira pochita uhule.

      Ndipo tsopano zinthu zimenezi zidzatengedwa kuti zikakhale malipiro a mahule kwinakwake.”

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani