Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Hoseya 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Chifukwa mayi awo amachita uhule.*+

      Mayi amene anatenga pakati nʼkuwabereka achita zinthu zochititsa manyazi+ ndipo anena kuti,

      ‘Nditsatira amuna ondikonda kwambiri+

      Ndiponso amene amandipatsa chakudya ndi madzi,

      Amandipatsanso zovala za ubweya wa nkhosa, nsalu, mafuta ndi zakumwa.’

  • Hoseya 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Usasangalale iwe Isiraeli.+

      Usachite zinthu mosangalala ngati anthu a mitundu ina.

      Popeza wasiya Mulungu wako chifukwa cha chiwerewere.+

      Umakonda kulandira malipiro a uhule wako pamalo onse opunthira mbewu.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani