Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • w17.03
  • Magazini Yophunzira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Magazini Yophunzira
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
w17.03
Nsanja ya Olonda Yophunzira, March 2017

Magazini Yophunzira

MARCH 2017

NKHANI ZOPHUNZIRA KUYAMBIRA MAY 1 MPAKA 28, 2017

© 2016 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

PATSAMBA LOYAMBA:

ROMANIA

Mkulu wina ndi mkazi wake akulalikira aneba awo amene akukonza ubweya wa nkhosa. Iwo amaona kuti Lamlungu akaweruka kumisonkhano imakhala nthawi yabwino yofufuza anthu amene ali ngati nkhosa, kumpoto kwa Romania.

KULI OFALITSA

40,575

MAPHUNZIRO A BAIBULO

25,623

OPEZEKA PA CHIKUMBUTSO (2015)

78,300

Magaziniyi sitigulitsa. Timaipereka ngati njira imodzi yophunzitsira anthu Baibulo padziko lonse ndipo ndalama zoyendetsera ntchitoyi ndi zimene anthu amapereka mwa kufuna kwawo.

Ngati mukufuna kupereka pitani pawebusaiti yathu ya www.jw.org/ny.

Malemba onse m’magaziniyi akuchokera mu Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika, lolembedwa m’Chichewa chamakono, kupatulapo ngati tasonyeza Baibulo lina.

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani