Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • w17.12
  • Magazini Yophunzira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Magazini Yophunzira
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
w17.12
Nsanja ya Olonda Yophunzira, December 2017

Magazini Yophunzira

December 2017

NKHANI ZOPHUNZIRA KUYAMBIRA: JANUARY 29–FEBRUARY 25, 2018

© 2017 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

PATSAMBA LOYAMBA:

CÔTE D’IVOIRE

M’dziko la Côte d’Ivoire (lomwe kale linkatchedwa Ivory Coast) mumalimidwa koko wambiri yemwe amagwiritsidwa ntchito popanga chokoleti. Kokoyo amayamba amuyanika padzuwa. Mpainiya akusonyeza mlimi mitu imene ili m’kabuku kakuti Uthenga Wabwino

KULI OFALITSA

11,133

MAPHUNZIRO A BAIBULO

28,274

OPEZEKA PA CHIKUMBUTSO (2016)

76,526

Magaziniyi sitigulitsa. Timaipereka ngati njira imodzi yophunzitsira anthu Baibulo padziko lonse ndipo ndalama zoyendetsera ntchitoyi ndi zimene anthu amapereka mwa kufuna kwawo.

Ngati mukufuna kupereka pitani pawebusaiti yathu ya www.jw.org/ny.

Malemba onse m’magaziniyi akuchokera mu Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika, lolembedwa m’Chichewa chamakono, kupatulapo ngati tasonyeza Baibulo lina.

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani