Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb17.09 4
  • September 11-17

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • September 11-17
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17.09 4

September 11-17

Ezekieli 46-48

  • Nyimbo Na. 134 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Aisiraeli Omwe Anachoka ku Ukapolo Analandira Madalitso”: (10 min.)

    • Ezek. 47:1, 7-12​—M’dziko lobwezeretsedwalo anthu anali ndi zokolola zambiri (w99 3/1 10 ¶11-12)

    • Ezek. 47:13, 14​—Banja lililonse linalandira cholowa chake (w99 3/1 10 ¶10)

    • Ezek. 48:9, 10​—Malo asanagawidwe kwa anthu, anaika padera gawo lina la malowo monga “chopereka” kwa Yehova

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Ezek. 47:1, 8; 48:30, 32-34​—N’chifukwa chiyani Ayuda amene anachokera ku ukapolo sankafunika kuona kukwaniritsidwa kwa mbali iliyonse ya masomphenya a Ezekieli onena za kachisi? (w99 3/1 11 ¶14)

    • Ezek. 47:6​—N’chifukwa chiyani Ezekieli akutchulidwa kuti ndi “mwana wa munthu”? (it-2 1001)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ezek. 48:13-22

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) wp17.5 chikuto​—Muuzeni zimene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) wp17.5​—Sonyezani mmene mungapangire ulendo wobwereza pogwiritsa ntchito magazini imene munamusiyira pa ulendo woyamba. Kenako musonyezeni limodzi mwa mabuku amene timagwiritsa ntchito pophunzira Baibulo.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bhs 35 ¶17​—Muitanireni kumisonkhano.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 28

  • Zofunika Pampingo: (8 min.) Mukhoza kukambirana zimene tikuphunzira mu Buku Lapachaka. (yb17 64-65)

  • Zimene Gulu Lathu Lachita: (7 min.) Onetsani vidiyo yakuti Zimene Gulu Lathu Lachita ya September.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 6 ¶16-24, komanso tsamba 67

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 11 ndi Pemphero

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani