Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb19.08 4
  • “Uike Akulu”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Uike Akulu”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mpingo wa Chikhristu Umayendetsedwa bwanji?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • Muziyamikira Amuna Amene Yehova Watipatsa Mumpingo
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19.08 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | TITO 1–FILIMONI

“Uike Akulu”

Tito 1:5-9

Tito akukambirana ndi abale

Paulo anauza Tito kuti ‘aike akulu mumzinda uliwonse.’ Zimenezi ndi zomwenso oyang’anira madera amachita akamaika akulu m’mipingo.

BUNGWE LOLAMULIRA

Potsatira zimene zinkachitika m’nthawi ya atumwi, Bungwe Lolamulira linapereka udindo wofunika kwambiri kwa oyang’anira madera woti aziika akulu komanso atumiki othandiza.

Mabokosi okonzedwa ngati mivi osonyeza mmene zinthu zimayendera

OYANG’ANIRA MADERA

Woyang’anira dera aliyense ayenera kuchita zinthu mosamala kwambiri komanso kupemphera asanaike munthu amene akulu amuvomereza kuti akhale paudindo.

Mabokosi okonzedwa ngati mivi osonyeza mmene zinthu zimayendera

AKULU

Ngakhale munthu ataikidwa paudindo, ayenera kupitirizabe kukwaniritsa ziyeneretso za m’Malemba.

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani