Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb18.08 2
  • Muzisonyeza Kuyamikira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzisonyeza Kuyamikira
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Tizisonyeza Kuti Ndife Oyamikira
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • “Mulungu Akuonetsa Chikondi Chake Kwa Ife”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Muzitsanzira Mtumwi Paulo pa Nkhani Yolalikira Komanso Kuphunzitsa
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18.08 2

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | LUKA 17-18

Muzisonyeza Kuyamikira

17:11-18

Akhate 10 anabwera kwa Yesu kudzapempha kuti awachiritse, koma atachiritsidwa, ndi mmodzi yekha amene anabwerera kudzathokoza

Kodi nkhani imeneyi ikutiphunzitsa chiyani pa nkhani yosonyeza kuyamikira?

  • Tisamangothokoza chamumtima koma tizichita zinthu zosonyeza kuti tikuyamikira

  • Munthu akamayamikira kuchokera pansi pa mtima amasonyeza kuti ali ndi makhalidwe abwino komanso amakonda Akhristu anzake

  • Anthu amene amafuna kusangalatsa Khristu amayesetsa kukonda komanso kuyamikira anthu onse, mosasamala kanthu kuti ndi osiyana nawo mtundu kapena chipembedzo

Kodi ndi liti pamene ndinayamikira munthu wina chifukwa chondithandiza?

Kodi ndi liti pamene ndinalemba kalata yosonyeza kuthokoza pa zimene wina anandichitira?

Mlongo akulemba kalata yothokoza
    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani