Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb18.09 5
  • Sipanawonongeke Chilichonse

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Sipanawonongeke Chilichonse
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Muzigwira Ntchito Yanu Mwaluso
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Pitirizani Kusonyeza Kuti Mumakonda Kwambiri Yehova
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Gawo 1
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • Mukhoza Kutumikira Yehova Ngakhale Makolo Anu Si Chitsanzo Chabwino
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18.09 5
Likulu la dziko lonse ku Warwick, New York

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Sipanawonongeke Chilichonse

Yesu atadyetsa mozizwitsa amuna oposa 5,000 kuphatikizapo akazi ndi ana, anauza ophunzira ake kuti: “Sonkhanitsani zotsala zonse, kuti pasawonongeke chilichonse.” (Yoh. 6:12) Yesu anasonyeza kuyamikira zimene Yehova anam’patsa, popewa kuwononga zinthu.

Masiku anonso, Bungwe Lolamulira limayesetsa kutsanzira Yesu pogwiritsa ntchito mosamala zinthu zimene abale ndi alongo amapereka. Mwachitsanzo, pomanga likulu lathu la padziko lonse, m’tawuni ya Warwick ku New York, abale anasankha pulani yabwino n’cholinga choti pasamadzaonongeke ndalama zambiri.

KODI TINGAPEWE BWANJI KUWONONGA ZINTHU . . .

  • M’bale akuthimitsa magetsi pa Nyumba ya Ufumu

    tikakhala pamisonkhano yachikhristu?

  • Wa Mboni za Yehova akulemba dzina lake m’Baibulo lake

    tikamatenga mabuku oti tizigwiritsa ntchito ifeyo? (km 5/09 3 ¶4)

  • M’bale akutenga timapepala tomwe akuona kuti tingamukwanire

    tikamatenga mabuku oti tizigwiritsa ntchito tikamalalikira? (mwb17.02 “Tizigwiritsa Ntchito Mwanzeru Mabuku Ndiponso Magazini” ¶1)

  • Mlongo akuonetsetsa kaye ngati mwininyumba ali ndi chidwi asanamugawire chilichonse

    tikakhala mu utumiki? (mwb17.02 4 ¶2, ndi bokosi)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani