Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb21.05 5
  • Muzikwaniritsa Zimene Mwalonjeza

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzikwaniritsa Zimene Mwalonjeza
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Nkhani Yofanana
  • “Uzikwaniritsa Zinthu Zimene Walonjeza”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Anthu Okhulupirika kwa Yehova Amakwaniritsa Zimene Alonjeza
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
  • Zimene Tingaphunzire pa Zomwe Zinkachitika pa Msasa wa Aisiraeli
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Utumiki wa Alevi
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21.05 5

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Muzikwaniritsa Zimene Mwalonjeza

Aisiraeli ankalonjeza zinthu mwakufuna kwawo koma ankafunika kukwaniritsa zimene alonjezazo (Nu 30:2; it-2 1162)

Malonjezo ena ankafuna kuti wolonjezayo azipewa zinthu zina ngakhale kuti zinthuzo sizolakwika (Nu 30:3, 4; it-2 1162)

Yehova masiku ano amachita zinthu ndi mtumiki wake aliyense payekha (Nu 30:6-9; w04 8/1 27 ¶3)

Malonjezo awiri ofunika kwambiri amene Mkhristu angapange masiku ano ndi lonjezo lokhudza kudzipereka kwa Mulungu komanso la ukwati.

Anthu akulonjeza. 1. Mtsikana akupemphera. 2. Mwamuna ndi mkazi akuvekana mphete pa ukwati wawo.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndikuchita zinthu zonse zomwe ndinalonjeza?’

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani