Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb21.11 22
  • Yefita Anali Munthu Wauzimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yefita Anali Munthu Wauzimu
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Nkhani Yofanana
  • Zimene Yefita Analonjeza
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Kusamvera Malamulo a Mulungu Kumabweretsa Mavuto
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Anthu Okhulupirika kwa Yehova Amakwaniritsa Zimene Alonjeza
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
  • Kodi Chilamulo Chinkasonyeza Bwanji Kuti Yehova Amaganizira Anthu Osauka?
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21.11 22

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Yefita Anali Munthu Wauzimu

Yefita sanasungire ena zifukwa (Owe 11:5-9; w16.04 7 ¶9)

Yefita ankaphunzira zimene Yehova ankachita ndi anthu ake (Owe 11:12-15; it-2 27 ¶2)

Yefita ankaganizira nkhani yofunika kwambiri yakuti Yehova ndiye Mulungu woona (Owe 11:23, 24, 27; it-2 27 ¶3)

Zithunzi: 1. M’bale akuwerenga Baibulo. 2. M’bale akulankhulana mwachikondi ndi mkazi wake. 3. M’bale ndi mkazi wake akhala pansi mwaulemu pamene anthu ena aimirira kuti achitire sailuti mbendera.

Kodi ndi zinthu ziti zimene ndimachita zomwe zimasonyeza kuti ndine munthu wauzimu?

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani