Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb22.01 10
  • Muzisonyeza Chikondi Chokhulupirika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzisonyeza Chikondi Chokhulupirika
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Pitirizani Kusonyezana Chikondi Chokhulupirika
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • “Kumene Inu Mupite Inenso Ndipita Komweko”
    Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo
  • Rute ndi Naomi
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Anali “Mkazi Wabwino Kwambiri”
    Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22.01 10

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Muzisonyeza Chikondi Chokhulupirika

[Onerani vidiyo yakuti Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Rute.]

Naomi anauza Olipa ndi Rute kuti abwerere ku Mowabu (Ru 1:8-13; w16.02 14 ¶5)

Rute anakana kusiya Naomi komanso Yehova (Ru 1:16, 17; w16.02 14 ¶6)

Zithunzi: 1. Amayi ndi mwana wawo akucheza ndi banja kudzera pa intaneti. 2. Banja lija latenga chakudya chophikaphika komanso basiketi momwe muli zakudya zina kupita nazo kwa amayi aja ndi mwana wawo.

Timasonyeza ena chikondi chokhulupirika ngati tili odzipereka, okhulupirika komanso ngati tili nawo pa ubwenzi wabwino. Yehova amasonyeza chikondi chokhulupirika kwa atumiki ake okhulupirika. (Sl 63:3) Ifenso tizisonyeza chikondi chokhulupirika kwa anthu ena.​—Miy 21:21.

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani