Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb22.09 14
  • “Kodi Mukayikakayika Mpaka Liti?”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Kodi Mukayikakayika Mpaka Liti?”
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Tizidalira Yehova Kuti Atilimbikitse
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • B8 Kachisi Amene Solomo Anamanga
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Zimene Tikuphunzira pa Nkhani ya Kulankhulana Bwino
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Sanasunthike pa Kulambira Koona
    Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22.09 14
Eliya, aneneri a Baala komanso anthu ena akuonerera pamene moto ukutsika kuchokera kumwamba n’kufika pa guwa la nsembe pomwe panali nsembe yopsereza.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

“Kodi Mukayikakayika Mpaka Liti?”

Eliya anauza Aisiraeli momveka bwino kuti anafunika kusankha zinthu mwanzeru (1Mf 18:21; w17.03 2:6)

Baala sanali mulungu wamoyo (1Mf 18:25-29; ia 10:15)

Yehova anasonyeza m’njira yodabwitsa kwambiri kuti ndi Mulungu weniweni (1Mf 18:36-38; ia 10:18)

Eliya anauza anthuwo kuti ankafunika kumvera Chilamulo cha Yehova kuti asonyeze kuti anali ndi chikhulupiriro. (De 13:5-10; 1Mf 18:40) Masiku ano timasonyeza kuti tili ndi chikhulupiriro komanso ndife odzipereka kwa Mulungu tikamamvera malamulo ake ndi mtima wonse.

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani