Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 81
  • Moyo wa Mpainiya

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Moyo wa Mpainiya
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Dzina Lanu Ndinu Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kufufuza Anthu Okonda Mtendere
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Titeteze Mtima Wathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 81

NYIMBO 81

Moyo wa Mpainiya

zosindikizidwa

(Mlaliki 11:6)

  1. 1. M’mawa uliwonse, tulo tisanathe,

    Timadzuka n’kupita

    kolalikira uthenga.

    Ndipo Mulungu amatitsogolera

    Timakondwa anthu

    akamamvetsera uthenga.

    (KOLASI)

    Tinasankha,

    kutumikira Yehova.

    Timachita zofuna zake.

    Tipitirizabe kulalikiraku,

    Tikatero timasonyeza

    Chikondi.

  2. 2. Pofika madzulo, timatopa ndithu,

    Komabe timapeza

    chimwemwe potumikira.

    Madalitso Yehova amatipatsa

    Nthawi zonse

    timamuthokoza potithandiza.

    (KOLASI)

    Tinasankha,

    kutumikira Yehova.

    Timachita zofuna zake.

    Tipitirizabe kulalikiraku,

    Tikatero timasonyeza

    Chikondi.

(Onaninso Yos. 24:15; Sal. 92:2; Aroma 14:8.)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani