Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb18.09 3
  • Yesu Analalikira Mayi Wachisamariya

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yesu Analalikira Mayi Wachisamariya
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Yesu Anakumana ndi Mayi Pachitsime
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki​—Mmene Mungayambire Kucheza ndi Anthu Kuti Muwalalikire Mwamwayi
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18.09 3
Yesu akuyankhula ndi mayi wachisamariya pachitsime; mayi wachisamariya akuuza ena za Yesu

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOHANE 3-4

Yesu Analalikira Mayi Wachisamariya

4:6-26, 39-41

Kodi n’chiyani chinathandiza Yesu kuti alalikire mwamwayi?

  • 4:7​—Iye anayamba n’kupempha madzi m’malo moyamba ndi kumufotokozera za Ufumu wa Mulungu kapena kumudziwitsa kuti iyeyo ndi Mesiya

  • 4:9​—Yesu sanachite tsankho kwa mayi wachisamariya chifukwa cha mtundu wake

  • 4:9, 12​—Mayiyo atayambitsa nkhani zimene zikanachititsa kuti asemphane maganizo, Yesu anapewa nkhanizo mwanzeru n’kupitirizabe kukambirana naye nkhani yofunikirayo.​—cf 77 ¶3

  • 4:10​—Iye anayamba ndi chitsanzo cha zimene mayiyo ankachita tsiku ndi tsiku

  • 4:16-19​—Ngakhale kuti mayiyu anali wachiwerewere, Yesu ankamulemekezabe

Kodi nkhaniyi ikusonyeza bwanji kufunika kolalikira mwamwayi?

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani