Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 40
  • Kodi Ndife a Ndani?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Ndife a Ndani?
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Ndinu ‘Okonzeka Kumvera’?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Mulungu Adzakulimbitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khalani Omvera Kuti Mulandire Madalitso
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tizikhulupirika Nthawi Zonse
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 40

NYIMBO 40

Kodi Ndife a Ndani?

zosindikizidwa

(Aroma 14:8)

  1. 1. Iwe ndi wandani?

    Umvera m’lungu uti?

    Amene umam’gwadirayo.

    Iye ndiye m’lungu wako.

    Milungu iwiri;

    Sungaitumikire.

    Sungalambire iwiri yonse,

    Sankhapo mmodzi yekha.

  2. 2. Iwe ndi wandani?

    Umvera m’lungu uti?

    Zilitu ndi iwe kusankha,

    Woona kaya wonama.

    Kodi Kaisara

    Udakamukondabe?

    Kapena udzamvera Yehova

    N’kugwira ntchito yake?

  3. 3. Ine ndi wandani?

    Ndidzamvera Yehova.

    Atate wanga wakumwamba;

    Ine ndidzam’sangalatsa.

    Anandigulatu;

    Ndidzamutumikira.

    Ndizim’lambira, dzina lakenso

    Ndizililemekeza.

(Onaninso Yos. 24:15; Sal. 116:14, 18; 2 Tim. 2:19.)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani