Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 144
  • Yang’ananibe Pamphoto

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yang’ananibe Pamphoto
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Musalole Kuti Chilichonse Chikulepheretseni Kulandira Mphoto
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Tizilalikira kwa Anthu a Mitundu Yonse
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Mulungu Watilonjeza Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 144

NYIMBO 144

Yang’ananibe Pamphoto

zosindikizidwa

(2 Akorinto 4:18)

  1. 1. Pomwe osaona ’kuwona

    Ovutika kumva akumva,

    Ana adzaimbanso nyimbo,

    Mtendere padziko lonse,

    Omwe anafa adzauka,

    Uchimo, mavuto zathanso,

    (KOLASI)

    Mudzaona zinthu zonsezi,

    M’kayang’anabe pamphoto.

  2. 2. Mimbulu idzadya ndi nkhosa,

    Zilombo zoopsa ndi ng’ombe,

    Mwana adzazitsogolera,

    Zidzamvera mawu ake.

    Pamene misozi idzatha,

    Mantha ndi zowawa zathanso,

    (KOLASI)

    Mudzaona zinthu zonsezi,

    M’kayang’anabe pamphoto.

(Onaninso Yes. 11:6-9; 35:5-7; Yoh. 11:24.)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani