Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 36
  • Titeteze Mtima Wathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Titeteze Mtima Wathu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Moyo wa Mpainiya
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Dzina Lanu Ndinu Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kufufuza Anthu Okonda Mtendere
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 36

NYIMBO 36

Titeteze Mitima Yathu

zosindikizidwa

(Miyambo 4:23)

  1. 1. Titeteze mtima wathu

    Tikhale ndi moyo.

    M’lungu amadziwa bwino

    Za mumtima mwathu.

    Mtima ndi wonyenga

    Ungamatisocheretse.

    Choncho tiganize bwino

    Timvere Yehova.

  2. 2. Timafunafuna M’lungu

    Tikamapemphera.

    Timathokozadi zonse

    Zomwe amachita.

    Zomwe amatiphunzitsa

    Timazitsatira

    Ndipo tikhulupirike,

    Timusangalatse.

  3. 3. Titeteze mtima wathu

    Tipewe zoipa.

    Mawu a Yehova M’lungu

    Atitsogolere.

    Anthu okhulupirika

    Amawakondadi.

    Choncho tizimulambira

    Monga bwenzi lathu.

(Onaninso Sal. 34:1; Afil. 4:8; 1 Pet. 3:4.)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani