33 Tsiku lililonse limene mudzabwere kudzaona malipiro+ anga, mudzaona chilungamo changa. Mukadzapeza mbuzi iliyonse yaikazi yopanda mathothomathotho kapena mawangamawanga, ndi nkhosa iliyonse yaing’ono yamphongo yomwe si yofiirira ili ndi ine, imeneyo ndiye kuti ndaba.”+