Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 21:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Poyankha Abulahamu anati: “Landirani ana a nkhosa aakazi 7 amene ndikukupatsaniwa, kuti akhale umboni+ wakuti ndinakumba chitsimechi ndine.”

  • Yoswa 22:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 koma kuti likhale mboni pakati pa ife+ ndi inu ndi mibadwo yobwera pambuyo pathu. Guwalo likhale mboni yakuti tidzatumikira Yehova pamaso pake ndi nsembe zathu zopsereza, nsembe zachiyanjano ndi nsembe zina,+ kuti tsiku lina m’tsogolo ana anu asadzanene kwa ana athu kuti: “Inu mulibe gawo mwa Yehova.”’

  • 3 Yohane 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Anthu onse amuchitira umboni Demetiriyo.+ Choonadinso chikumuchitira umboni. Ifenso tikuchitira umboni,+ ndipo iwenso ukudziwa kuti umboni umene timapereka ndi woona.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena