Oweruza 11:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Poyankha akulu a ku Giliyadi anauza Yefita kuti: “Yehova amve makambirano athuwa+ ndi kutiweruza ngati sitidzachita zogwirizana ndi mawu ako.”+ 1 Samueli 12:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Atatero, iye anawayankha kuti: “Yehova ndi mboni yokutsutsani, ndipo wodzozedwa+ wake ndi mboni lero kuti simunandipeze ndi mlandu uliwonse.”+ Pamenepo iwo anati: “Inde, iyedi ndi mboni.” Malaki 2:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Inu mwanena kuti, ‘Chifukwa chiyani?’+ Chifukwa chakuti Yehova wakudzudzulani popeza kuti aliyense wa inu wachitira zachinyengo mkazi amene anamukwatira ali mnyamata,+ ngakhale kuti iye anali mnzake komanso mkazi wa pangano lake.+
10 Poyankha akulu a ku Giliyadi anauza Yefita kuti: “Yehova amve makambirano athuwa+ ndi kutiweruza ngati sitidzachita zogwirizana ndi mawu ako.”+
5 Atatero, iye anawayankha kuti: “Yehova ndi mboni yokutsutsani, ndipo wodzozedwa+ wake ndi mboni lero kuti simunandipeze ndi mlandu uliwonse.”+ Pamenepo iwo anati: “Inde, iyedi ndi mboni.”
14 Inu mwanena kuti, ‘Chifukwa chiyani?’+ Chifukwa chakuti Yehova wakudzudzulani popeza kuti aliyense wa inu wachitira zachinyengo mkazi amene anamukwatira ali mnyamata,+ ngakhale kuti iye anali mnzake komanso mkazi wa pangano lake.+