Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 1:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Tsopano Mulungu anati: “Taonani, ndakupatsani zomera zonse zobala mbewu zapadziko lonse lapansi, ndi mitengo yonse yobala zipatso za mbewu+ kuti zikhale chakudya chanu.+

  • Salimo 72:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Padziko lapansi padzakhala tirigu wambiri.+

      Pamwamba pa mapiri padzakhala tirigu wochuluka.+

      Zokolola za mfumu zidzachuluka ngati mitengo ya ku Lebanoni,+

      Ndipo anthu ochokera mumzinda adzaphuka ngati udzu wa panthaka.+

  • Mateyu 13:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Kanjere kameneka ndi kakang’ono kwambiri mwa njere zonse, koma kakamera kamakula kwambiri kuposa mbewu zonse zakudimba ndipo umakhala mtengo, moti mbalame zam’mlengalenga+ zimabwera kudzapeza malo okhala munthambi zake.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena