Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 2:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Yehova Mulungu anali kuumba ndi dothi nyama iliyonse yakutchire, ndi cholengedwa chilichonse chouluka m’mlengalenga. Ndipo anayamba kuzibweretsa kwa munthuyo, kuti chilichonse achitche dzina. Dzina lililonse limene munthuyo anatchula chamoyo chilichonse,+ limenelo linakhaladi dzina lake.+

  • Genesis 9:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 komanso ndi chamoyo chamtundu uliwonse chimene muli nacho limodzi, pakati pa mbalame ndi pakati pa nyama zonse zamoyo za padziko lapansi, kuyambira zonse zotuluka m’chingalawa, kufikira cholengedwa chamoyo chilichonse cha padziko lapansi.+

  • Deuteronomo 4:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 chifaniziro cha nyama iliyonse ya padziko lapansi,+ chifaniziro cha mbalame iliyonse youluka m’mlengalenga,+

  • Yobu 12:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Koma funsa nyama zoweta ndipo zikulangiza.+

      Komanso zouluka zam’mlengalenga, ndipo zikuuza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena