Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 16:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pambuyo pake, mngelo wa Yehova+ anakapeza Hagara m’chipululu ali pakasupe wamadzi wa panjira yopita ku Shura.+

  • Oweruza 13:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Mngelo wa Yehova uja sanaonekerenso kwa Manowa ndi mkazi wake. Pamenepo Manowa anadziwa kuti anali mngelo wa Yehova.+

  • Machitidwe 7:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Sitefano anati: “Amuna inu, abale anga ndi abambo anga, mvetserani! Mulungu waulemerero+ anaonekera kwa kholo lathu Abulahamu pamene anali ku Mesopotamiya, asanakakhale ku Harana.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena