Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 15:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pamenepo Yehova anamuuza kuti: “Munthu ameneyu sadzakhala wolowa nyumba yako ayi, koma munthu amene adzatuluke mwa iwe ndi amene adzakhale wolowa nyumba yako.”+

  • Yohane 8:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Komanso, kapolo sakhala m’banjamo kwamuyaya, mwana ndiye amakhalamo kwamuyaya.+

  • Agalatiya 4:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ngakhale zili choncho, kodi Malemba amati chiyani? “Thamangitsani mdzakaziyu pamodzi ndi mwana wakeyu pano, pakuti sizingatheke mwana wa mdzakazi kudzakhala wolandira cholowa pamodzi ndi mwana wa mkazi waufulu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena