Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 4:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Zitatero, Yehova anamukwiyira kwambiri Mose ndipo anati: “Kodi Aroni Mlevi si m’bale wako?+ Ndikudziwa kuti amatha kulankhula. Ndiponso, iye ali m’njira kudzakuchingamira. Akakuona, adzakondwera kwambiri mumtima mwake.+

  • Salimo 99:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Mose ndi Aroni anali pakati pa ansembe ake,+

      Samueli anali pakati pa anthu amene anali kuitana pa dzina lake.+

      Iwo anali kuitana Yehova, ndipo iye anali kuwayankha.+

  • Aheberi 5:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Komanso, munthu amalandira ulemu umenewu, osati mwa kufuna kwake,+ koma mwa kuchita kuitanidwa ndi Mulungu,+ monga mmene anaitanira Aroni.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena